LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

d Kuonongedwa kwa Babulo n’citsanzo cimodzi cabe ca maulosi a m’Baibo amene anakwanilitsika kale. Zitsanzo zina ndi za kuonongedwa kwa mzinda wa Turo ndi wa Nineve. (Ezekieli 26:1-5; Zefaniya 2:13-15) Ndiponso, ulosi wa Danieli unakambilatu za maulamulilo amphamvu a padziko amene anali kudzakhalapo motsatizana pambuyo pa ulamulilo wa Babulo. Maulamulilo amenewa anaphatikizapo maulamulilo a Amedi ndi Aperisiya, ndi wa Gilisi. (Danieli 8:5-7, 20-22) Onani Zakumapeto, pamapeji 199 mpaka 201, kuti mudziŵe maulosi ambili onena za Mesiya amene anakwanilitsika mwa Yesu Kristu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani