LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Yehova amachedwa kuti Atate cifukwa iye ndiye Mlengi. (Yesaya 64:8) Popeza kuti Yesu analengedwa ndi Mulungu, amachedwa Mwana wa Mulungu. Pa cifukwa cimodzi-modzi, zolengedwa zinanso zauzimu zimachedwa ana a Mulungu. Koma Adamu nayenso amachedwa mwana wa Mulungu.—Yobu 1:6; Luka 3:38.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani