LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Apa sititanthauza kuti aliyense amene angakutsutseni ndiye kuti amatsogoleledwa ndi Satana mwacindunji. Koma Satana ndiye Mulungu wa dongosolo lino la zinthu, ndipo dziko lonse lili m’manja mwake. (2 Akorinto 4:4; 1 Yohane 5:19) Mwa ici, anthu ena sadzatikonda cifukwa cokhala ndi umoyo wokondweletsa Mulungu, ndipo ena adzatitsutsa.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani