LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Baibulo limaonetsa kuti, kungokhala ndi cikumbumtima coyela sikokwanila. Mwacitsanzo, mtumwi Paulo anati: “Sindikudziŵa kanthu kalikonse konditsutsa mumtima mwanga. Koma zimenezi sizikutanthauza kuti basi ndine wolungama, koma Yehova ndiye amandifufuza.” (1 Akorinto 4:4) Ngakhale anthu amene amazunza Akristu, monga mmene Paulo anali kucitila, angacite zimenezo ndi cikumbumtima coyela, ndi kumaganiza kuti Mulungu amavomeleza zocita zao. Conco, n’kofunika kuti cikumbumtima cathu cikhale coyela kwa ife ndi kwa Mulungu.—Machitidwe 23:1; 2 Timoteyo 1:3.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani