Mawu Amunsi
a Nthawi zina, Mkristu angacitile Mkristu mnzake colakwa cacikulu monga kugona naye mwacikakamizo, kumumenya, kumupha, kapena kumubela zinthu. Zotelo zikacitika, sikulakwa kupeleka nkhaniyo kupolisi ngakhale kuti kucita zimenezo kungapangitse kuti nkhaniyo ikafike kukhoti.