LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Asayansi amakamba kuti pamene anthufe tikula timayamba kukhala ndi mphamvu yotithandiza kudziŵa pamene pali manja ndi miyendo yathu. Mwacitsanzo, mphamvu imeneyi imakuthandizani kuomba m’manja ngakhale pamene mwatseka maso anu. Wodwala wina amene mphamvu imeneyi inaonongeka, anali kulephela kuimilila, kuyenda ngakhale kukhala tsonga.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani