LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Ayuda ocokela kutali anali kufunikila kugwilitsila nchito ndalama zovomelezeka kuti apeleke msonkho wapacaka pakacisi, ndipo osintha ndalama anali kulipilitsa anthu ofuna kusinthitsa ndalamawo. Alendowo ayenelanso kuti anali kugula nyama kuti apeleke nsembe. Yesu anacha amalondawo kuti “acifwamba” mwina cifukwa cakuti io anali kubela anthu powalipilitsa ndalama zambili akafuna kusinthitsa ndalama zao kapena kugula nyama.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani