Mawu Amunsi
c Katswili wina anakamba kuti mau acigiriki amene anawamasulila kuti “watsimikizila” amatanthauza kuti “munthuyo amayamba waganizila coyamba.” Iye ananenanso kuti: “Ngakhale kuti kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka, tiyenela kuganizila ndi kulinganiza copeleka cathu pasadakhale.”—1 Akor. 16:2.