Mawu Amunsi
a Pano sititanthauza kuti Satana ndiye amangena mwa anthu amene amayesa kukuletsani kuphunzila Baibulo, iyai. Koma mfundo yake ni yakuti, Satana ni “mulungu wa nthawi ino,” ndipo ‘dziko lonse lili m’manja mwake.’ Conco tisadabwe ngati anthu ena ayesa kutilepheletsa kutumikila Yehova.—2 Akorinto 4:4; 1 Yohane 5:19.