LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Pano sititanthauza kuti Satana ndiye amangena mwa anthu amene amayesa kukuletsani kuphunzila Baibulo, iyai. Koma mfundo yake ni yakuti, Satana ni “mulungu wa nthawi ino,” ndipo ‘dziko lonse lili m’manja mwake.’ Conco tisadabwe ngati anthu ena ayesa kutilepheletsa kutumikila Yehova.—2 Akorinto 4:4; 1 Yohane 5:19.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani