Mawu Amunsi
a Anthu osweka mtima Yehova amasamala za iwo. (Salimo 34:18) Iye amamvetsa maganizo osautsa amene angapangitse munthu kufuna kudzipha, ndipo amafuna kuwathandiza anthu otelo. Kuti muone mmene iye amathandizila, ŵelengani nkhani yakuti “Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?” pa mbali yakuti Fufuzani m’phunzilo lino.