Mawu Amunsi
b Pali zipatala zambili ndiponso malo ena othandizila anthu amene ali na vuto lomwa moŵa mwaucidakwa. Nsanja ya M’londa sisankhila anthu mankhwala. Aliyense ayenela kufufuza bwino za mankhwala n’kusankha yekha mankhwala amene satsutsana na zimene Baibo imaphunzitsa