LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Malinga ndi lemba la Machitidwe 20:29, 30, Paulo anafotokoza kuti mkati mwa mpingo wacikristu “anthu ena adzayamba kulankhula zinthu zopotoka kuti apatutse ophunzila aziwatsatila.” Mbili yakale imatsimikizila kuti m’kupita kwa nthawi, panakhala kusiyana pakati pa akulu-akulu a chalichi ndi anthu wamba. Pofika m’zaka za m’ma 200 C.E., “munthu wosamvela malamulo” anaonekela kukhala gulu la atsogoleli a Machalichi Acikristu.—Onani Nsanja ya Olonda ya February 1, 1990, tsamba 10 mpaka 14.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani