LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Ofufuza ena anafotokoza kuti abale ake a Yosefe anaona kuti mphatso imene bambo wao anapatsa Yosefe inapeleka umboni wonena kuti iye anali kufuna kuti mnyamatayo alandile ufulu wa mwana woyamba kubadwa. Iwo anadziŵa kuti Yosefe anali mwana woyamba kubadwa kwa mkazi wake wokondedwa—amene anafunika kukwatila paciyambi. Patapita nthawi, Rubeni mwana woyamba wa Yakobo anagona ndi Biliha mkazi wacinai wa atate ake, ndiyeno anacititsa manyazi atate ake ndipo mwacionekele anataya mwai wokhala mwana woyamba kubadwa kapena wamkulu.—Genesis 35:22; 49:3, 4.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani