Mawu Amunsi
b Ngakhale ndi mau ocepa amenewa, Baibulo limaonetsa kuti zimenezi n’zoona. Nkhani zolembedwa za m’nthawi imeneyo zionetsa kuti munthu anali kugulitsidwa ndi kupita ku ukapolo ku Iguputo ndi masekeli 20.
b Ngakhale ndi mau ocepa amenewa, Baibulo limaonetsa kuti zimenezi n’zoona. Nkhani zolembedwa za m’nthawi imeneyo zionetsa kuti munthu anali kugulitsidwa ndi kupita ku ukapolo ku Iguputo ndi masekeli 20.