LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

g Ponena za ulosi wokhudza masiku otsiliza Yesu anati: “Anthu amitundu ina adzapondaponda Yerusalemu [amene akuimila ulamulilo wa Mulungu], kufikila nthawi zoikidwilatu za anthu amitundu inawo zitakwanila.” (Luka 21:24) Conco tinganene kuti kusokonezedwa kwa ulamulilo wa Mulungu kunali kudakalipo pamene Yesu anali padziko lapansi ndipo kunayenela kupitilizabe mpaka m’masiku otsiliza.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani