Mawu Amunsi
b Mulungu anasamutsa moyo wa mwana wake ndi kuuika m’mimba mwa Mariya, ndipo iye anakhala ndi pakati. Mzimu woyela wa Mulungu unateteza Yesu kuti asatengele kupanda ungwilo kwa Mariya.—Luka 1:31, 35.
b Mulungu anasamutsa moyo wa mwana wake ndi kuuika m’mimba mwa Mariya, ndipo iye anakhala ndi pakati. Mzimu woyela wa Mulungu unateteza Yesu kuti asatengele kupanda ungwilo kwa Mariya.—Luka 1:31, 35.