Mawu Amunsi
b Mwacitsanzo, cikalata ca boma la United States coonetsa kuti dzikolo lalandila ufulu wodzilamulila cinalembedwa pa cikumba ca nyama. Koma tsopano n’cowonongeka kwambili cakuti mawu ambili anafutika ngakhale kuti papita zaka zosakwana 250.