Mawu Amunsi
a Nthawi zina zitsulo zimenezo zinali kukhala zokhota ngati cikwakwa. Zitsulozo ziyenela kuti zinali kukhala m’mbali mwa magaleta, ndipo mwina anali kuzimangilila ku mahabu a mawilo. Analidi magaleta a nkhondo ocititsa mantha kuwayandikila.