Mawu Amunsi
c “Kubala zipatso” kungatanthauzenso kukhala na “makhalidwe amene mzimu woyela” umabala. Koma m’nkhani ino na yokonkhapo, tidzakambilana kwambili za kubala “cipatso ca milomo yathu” kapena kuti kulengeza uthenga wabwino wa Ufumu.—Agal. 5:22, 23; Aheb. 13:15.