LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b MAWU OFOTOKOZEDWA: Kufatsa. Munthu wofatsa amakhala wokoma mtima pocita zinthu ndi ena, ndipo amakhalabe wodekha ngakhale pamene ena amukhumudwitsa. Kudzicepetsa. Munthu wodzicepetsa sakhala wonyada kapena wodzikuza. Koma amaona ena kukhala om’posa. Yehova ni wodzicepetsa m’lingalilo lakuti, ngakhale ni wapamwamba kwambili, amacita zinthu mwacikondi komanso mwacifundo ndi anthu komanso angelo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani