Mawu Amunsi
c MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: Mwamuna amene akupita ku chuti watenga kathilakiti kwa Mboni za Yehova pa eyapoti. Ali ku chutiko, waonanso Mboni zina zili pa ulaliki wa poyela. Atabwelela ku nyumba, Mboni zinanso zabwela pa nyumba kukam’lalikila.