LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b KUFOTOKOZELA MAWU ENA: Kudzozedwa na mzimu woyela: Yehova amaseŵenzetsa mzimu wake woyela kusankha anthu amene adzalamulila na Yesu kumwamba. Poseŵenzetsa mzimu wake, iye amapatsa anthuwo lonjezo la zinthu zakutsogolo kapena kuti ‘cikole ca colowa cawo cam’tsogolo.’ (Aef. 1:13, 14) Ndiye cifukwa cake Akhristu amenewa angakambe kuti mzimu woyela ‘umawacitila umboni,’ kapena kuti kuwatsimikizila kuti adzalandila mphoto yakumwamba.—Aroma 8:16.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani