Mawu Amunsi
a Tidziŵa kuti Atate wathu Yehova amatikonda kwambili, ndipo watibweletsa m’banja la olambila ake. N’cifukwa cake nafenso timam’konda. Kodi tingaonetse bwanji kuti timam’kondadi Yehova Atate wathu? M’nkhani ino, tikambilana zina zimene tingacite kuti tionetse kuti timam’konda.