LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kuti banja liyende bwino, aliyense m’banjamo ayenela kudziŵa udindo wake, komanso kulimbikitsa mgwilizano. Tate ayenela kutsogolela banjalo mwacikondi, mayi ayenela kucilikiza mwamuna wake, ndipo ana ayenela kumvela makolo awo. Ni mmenenso zilili m’banja la Yehova. Mulungu wathu ali nafe colinga, ndipo ngati ticita zinthu mogwilizana na colingaco, tidzakhala m’banja la alambili ake kwamuyaya.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani