LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kodi munamvelapo munthu amene watumikila Yehova kwanthawi yaitali akukamba kuti, ‘Sin’naganizilepo kuti ningafike msinkhu uno mapeto asanacitike? Tonsefe timafuna kuti Yehova awononge dziko loipali, maka-maka m’nthawi zino zovuta. Komabe, tiyenela kukhala oleza mtima. M’nkhani ino, tikambilane mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kuyembekezela moleza mtima. Tikambilanenso mbali ziŵili zimene zifuna kuti tiyembekezele Yehova moleza mtima. Cotsilizila, tiona madalitso amene anthu oyembekezela pa Yehova adzapeza.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani