LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yehova timam’konda kwambili, ndipo timafuna kucita zonse zotheka pom’tumikila. Ndiye cifukwa cake, timafunitsitsa kuwonjezela utumiki wathu, komanso kukalamila maudindo owonjezeleka mu mpingo. Nanga bwanji ngati mwayesetsa kucita zonse zotheka kuti mukwanilitse zolinga zanu, koma zalepheleka? Kodi n’ciani cingatithandize kupitiliza kukhala okangalika, komanso acimwemwe? Tipeza yankho m’fanizo la Yesu la matalente.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani