Mawu Amunsi
a Cifundo ni khalidwe limodzi mwa makhalidwe a Yehova abwino ngako, komanso limene tonsefe tiyenela kukulitsa. M’nkhani ino, tikambilane cifukwa cake Yehova amaonetsa cifundo, ndiponso cifukwa cake tingakambe kuti cilango cake cimaonetsa cifundo. Tikambilanenso mmene tingaonetsele acifundo monga Yehova.