Mawu Amunsi
a Zisankho zina zimene timapanga zingakhudze nthawi na mphamvu zathu potumikila Yehova. Amene akwatilana posacedwa angafunike kupanga zisankho zimene zingakhudze umoyo wawo kwa nthawi yaitali. Nkhani ino, idzawalimbikitsa kupanga zisankho zimene zingawathandize kukhala na umoyo wopindulila.