LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c Kumbuyoko, zofalitsa zathu zinali kufotokoza kuti mawu akuti ‘kuweluza’ pa lembali atanthauza ciweluzo copeleka cilango. N’zoona kuti mawu amenewa angatanthauze zimenezi. Koma pa lembali, zioneka kuti Yesu anagwilitsa nchito mawu amenewa akuti ‘kuweluza’ potanthauza kuunika munthu na kumuyang’anila, kapena kuti “kusanthula khalidwe lake,” malinga na dikishonale ina ya Cigiriki.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani