LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Mwina ciukitso cidzayamba na anthu amene anamwalila ali okhululupillika m’masiku otsiliza ano, kenako kutsatila mibadwo mibadwo kubwelela m’mbuyo. Ngati zidzakhaladi conco, ndiye kuti m’badwo uliwonse udzakhala na mwayi wolandila anthu oukitsidwa amene anali kuwadziŵa. Mulimonsemo, ponena za ciukitso ca anthu opita kumwamba, Malemba amakamba kuti “aliyense pamalo pake.” Conco, zioneka kuti naconso ciukitso ca anthu pano padziko lapansi cidzacitika mwadongosolo.—1 Akor. 14:33; 15:23.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani