Mawu Amunsi
a M’nkhani ino, tikambilane zinthu zitatu zimene zinathandiza mneneli Ezekieli kugwila nchito yolalikila imene anapatsidwa. Pokambilana mmene Yehova anathandizila mneneli wake ameneyu, tidzalimbitsa cidalilo cathu cakuti Yehova adzatithandiza nafenso kugwila nchito yathu yolalikila.