Mawu Amunsi
d Cilamulo cinafuna kuti mutu wa banja akafuna kupha nyama kuti adye na banja lake, nyamayo anafunika kuitenga kupita nayo ku malo opatulika, kupatulapo ngati akukhala kutali na malo opatulikawo.—Deut. 12:21.
d Cilamulo cinafuna kuti mutu wa banja akafuna kupha nyama kuti adye na banja lake, nyamayo anafunika kuitenga kupita nayo ku malo opatulika, kupatulapo ngati akukhala kutali na malo opatulikawo.—Deut. 12:21.