Mawu Amunsi
a Kodi mukuyembekezela kudzakhala na moyo kwamuyaya? Yehova anatilonjeza kuti m’tsogolo tidzakhala na moyo popanda kudelanso nkhawa kuti tsiku lina tidzafa. M’nkhani ino, tikambilane zifukwa zimene tingakhalile na cidalilo conse kuti Yehova adzakwanilitsa malonjezo ake.