Mawu Amunsi
a Nthawi zambili, Yehova amagwilitsa nchito atumiki ake okhulupilika kuti athandize aja amene akukumana na mavuto. Angaseŵenzetse inu kuti mulimbikitse abale na alongo anu. Tiyeni tione mmene tingathandizile ena akafunikila thandizo.
a Nthawi zambili, Yehova amagwilitsa nchito atumiki ake okhulupilika kuti athandize aja amene akukumana na mavuto. Angaseŵenzetse inu kuti mulimbikitse abale na alongo anu. Tiyeni tione mmene tingathandizile ena akafunikila thandizo.