LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Mtumwi Paulo analimbikitsa Akhristu anzake kusalola dongosolo lino la zinthu kuumba kaganizidwe kawo. Uwu ni uphungu wabwino ngakhale kwa ife masiku ano. Tiyenela kuyesetsa kusalola maganizo oipa a dzikoli kuumba kaganizidwe kathu mwa njila ina iliyonse. Kuti izi zitheke, tiyenela kupitiliza kuwongolela kaganizidwe kathu, nthawi zonse tikazindikila kuti sikogwilizana na cifunilo ca Mulungu. M’nkhani ino, tikambilane mmene tingacitile zimenezi.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani