Mawu Amunsi
f Patapita zaka zambili, rabi wina anati: “M’dzikoli anthu olungama monga Abulahamu alimo osacepela 30. Ngati alipo 30, ine na mwana wanga ndife ena mwa iwo. Ngati alipo 10, ine na mwana wanga tili pakati pawo. Ngati alipo asanu, ine na mwana wanga tili pakati pawo. Ngati alipo aŵili, ndine na mwana wanga. Ngati alipo mmodzi, ameneyo ndine.”