Mawu Amunsi
a M’Baibo, liwu lakuti “kuopa” lili na matanthauzo ambili. Malinga na nkhani yake, lingatanthauze kucita mantha kwambili, kupeleka ulemu, kapena kucita nthumanzi. M’nkhani ino, tikambilane mantha amene angatithandize kukhala olimba mtima, komanso okhulupilika potumikila Atate wathu wakumwamba.