Mawu Amunsi
a Samisoni ni dzina la munthu wa m’Baibo amene ni wodziŵika kwambili ngakhale kwa anthu osadziŵa zambili za m’Baibo. Nkhani yake aifotokozapo m’maseŵelo, nyimbo komanso m’mafilimu. Ngakhale n’telo, nkhaniyi si nthano cabe. Tingaphunzile zambili kwa mwamuna wa cikhulupililo ameneyu.