Mawu Amunsi
a Mungapeze mfundo zolimbikitsa cikhulupililo pa jw.org mwa kulemba mu danga lofufuzila mawu akuti “tsanzirani cikhulupiriro cawo” kapena “zocitika”. Mu JW Library®, mungapeze nkhanizi pansi pa kamutu kakuti article series zolembedwa kuti “Mbiri ya Mboni za Yehova Zosiyanasiyana” kapena “Tsanzirani Cikhulupirilo Cawo” m’Chichewa.