Mawu Amunsi
e MAWU OFOTOKOZELA CITHUNZI: M’bale amene anamangidwa cifukwa ca cikhulupililo cake akusinkhasinkha mmene Yehova anamuthandizila kuleka kukoka fodya, mmene akumulimbikitsila kupitila m’makalata ocokela kwa okondeka ake, komanso mmene adzamupatsile moyo wosatha m’Paradaiso.