Mawu Amunsi
a MAWU OFOTOKOZELA CITHUNZI: Cithunzi coyelekezela abale athu mu ulamulilo wakale wa Soviet Union, atalandila kalata yooneka ngati yacokela kulikulu lathu, pomwe m’ceniceni inacokela kwa adani athu. Masiku anonso, adani athu angaseŵenzetse intaneti pofalitsa nkhani zabodza zokhudza gulu la Yehova.