LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Mmene mawu a Ciheberi anawagwilitsila nchito palembali aonetsa kuti uku ndiye kukhululuka kwenikweni. Amaonetsanso kuti ndi Yehova yekhayo amene angakhululuke macimo ndi mtima wonse. Mu Mabaibulo ambili mulibe mfundo yofunika imeneyi palembali, koma mu Baibulo la Dziko Latsopano ilimo. Izi zimapangitsa Baibulo limeneli kukhala lapadela m’njila imene anamasulila lemba la Salimo 130:4.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani