Mawu Amunsi
a Zioneka kuti ciwanda n’cimene cinapangitsa Elifazi kukamba kuti Yehova saona anthu kukhala olungama, ndipo palibe munthu angakondweletse Mulungu. Elifazi anaikhulupilila kwambili mfundo yopotoka imeneyi ndipo nthawi zonse akamalankhula ndi Yobu, anali kuibweleza.—Yobu 4:17; 15:15, 16; 22:2.