LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Zioneka kuti ciwanda n’cimene cinapangitsa Elifazi kukamba kuti Yehova saona anthu kukhala olungama, ndipo palibe munthu angakondweletse Mulungu. Elifazi anaikhulupilila kwambili mfundo yopotoka imeneyi ndipo nthawi zonse akamalankhula ndi Yobu, anali kuibweleza.​—Yobu 4:17; 15:​15, 16; 22:2.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani