Mawu Amunsi
a KUFOTOKOZELA MAU ENA: M’zikhalidwe zambili, ukwati umaphatikizapo mwambo wolumbilitsa mwamuna ndi mkazi amene akukwatilana. Iwo amalumbila kuti adzakhala limodzi kwa moyo wao wonse. Pambuyo pake, pangakhale phwando la ukwati. Anthu amene amakhala m’madela amene anthu sacita mwambo wa ukwati kapena phwando la ukwati, angapindulebe mwa kutsatila mfundo za m’Baibo pa tsiku la ukwati wao.