LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Zikuoneka kuti anthu ambili m’gulu limenelo anakhala Akristu. Takamba conco cifukwa cakuti mtumwi Paulo anawachula kuti “abale 500.” Iye anakambanso kuti: “Ambili a io akali ndi moyo mpaka lelo, koma ena anagona mu imfa.” Motelo, zioneka kuti Paulo ndi Akristu ena anali kuwadziŵa anthu ambili amene anamva mwacindunji pamene Yesu anali kulamula ophunzila ake kuti azilalikila.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani