Mawu Amunsi
b Baibo imatilamula kuti tiyenela “kupitiliza kupewa . . . magazi.” (Machitidwe 15:28, 29) Izi zitanthauza kuti sitiyenela kumwa magazi kapena kudya nyama yosakhetsa, ndipo sitiyenela kudya cakudya ciliconse cosakanizidwa na magazi.
b Baibo imatilamula kuti tiyenela “kupitiliza kupewa . . . magazi.” (Machitidwe 15:28, 29) Izi zitanthauza kuti sitiyenela kumwa magazi kapena kudya nyama yosakhetsa, ndipo sitiyenela kudya cakudya ciliconse cosakanizidwa na magazi.