Mawu Amunsi
b Mwacitsanzo, nkhani ina m’magazini yochedwa Marriage & Family Review inati: “Anthu ena anapanga kafuku-fuku maulendo atatu ndipo anapeza kuti anthu ambili amene akhala pa banja nthawi yaitali (zaka 25 mpaka 50 kapena zoposa) ni amene ali m’cipembedzo cimodzi ndipo amakhulupilila zofanana.”—voliyumu 38, magazini yoyamba, peji 88 (2005).