Mawu Amunsi
a Dipatimenti Yoona za Mapulani na Zomanga-manga (LDC) imapanga mapulani na kutsogolela pa nchito yomanga Nyumba za Ufumu m’dela la nthambi yawo. Dipatimenti Yoona za Mapulani na Zomanga-manga Padziko Lonse, imene ili ku likulu la padziko lonse, imaona nchito zimene zingakhale zoyambilila kugwilidwa na mmene angazigwilile.