Mawu Amunsi
a Maphunzilo a sukuluyi amakonzedwa na Dipatimenti ya Maphunzilo a Zaumulungu, imene imayang’anilidwa na Komiti Yoyang’anila Nchito Yophunzitsa ya Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova. Amene amaphunzitsa sukuluyi ni alangizi ocokela m’Dipatimenti ya Maphunzilo a Zaumulungu komanso alangizi ena, kuphatikizapo abale a m’Bungwe Lolamulila.