Mawu Amunsi
c Cifukwa ca ziletso zokhudzana na mlili wa COVID-19, abale athu anafunika kutenga zilolezo kuti akapeleke zakudya. Analinso osamala kwambili kuti asakhale pa ciopsezo cotenga kalombo koyambitsa matenda amenewa.
c Cifukwa ca ziletso zokhudzana na mlili wa COVID-19, abale athu anafunika kutenga zilolezo kuti akapeleke zakudya. Analinso osamala kwambili kuti asakhale pa ciopsezo cotenga kalombo koyambitsa matenda amenewa.